Yohane 21:14 - Buku Lopatulika14 Imeneyo ndi nthawi yachitatu yakudzionetsera Yesu kwa ophunzira ake, m'mene atauka kwa akufa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Imeneyo ndi nthawi yachitatu yakudzionetsera Yesu kwa ophunzira ake, m'mene atauka kwa akufa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Aka nkachitatu kuti Yesu aonekere ophunzira ake Iye atauka kwa akufa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Aka kanali tsopano kachitatu Yesu akuonekera kwa ophunzira ake Iye ataukitsidwa kwa akufa. Onani mutuwo |