Yohane 20:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti kufikira pomwepo sanadziwe lembo lakuti ayenera Iye kuuka kwa akufa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti kufikira pomwepo sanadziwa lembo lakuti ayenera Iye kuuka kwa akufa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Mpaka nthaŵi imeneyo iwo aja anali asanamvetse Malembo akuti Yesu adzayenera kuuka kwa akufa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 (Iwo sanazindikire kuchokera mʼmalemba kuti Yesu anayanera kuuka kuchokera kwa akufa). Onani mutuwo |