Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 20:10 - Buku Lopatulika

10 Chifukwa chake ophunzirawo anachokanso, kunka kwao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Chifukwa chake ophunzirawo anachokanso, kunka kwao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Pambuyo pake ophunzirawo adabwerera kwao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Kenaka ophunzira anabwerera ku nyumba zawo,

Onani mutuwo Koperani




Yohane 20:10
4 Mawu Ofanana  

Koma Petro ananyamuka nathamangira kumanda, ndipo powerama anaona nsalu zabafuta pazokha; ndipo anachoka nanka kwao, nazizwa ndi chija chidachitikacho.


Onani ikudza nthawi, ndipo yafika, imene mudzabalalitsidwa, yense ku zake za yekha, ndipo mudzandisiya Ine pa ndekha. Ndipo sindikhala pa ndekha, chifukwa Atate ali pamodzi ndi Ine,


Koma Maria analikuima kumanda kunja, alikulira. Ndipo m'mene alikulira anawerama chisuzumirire kumanda;


Ndipo anamuka munthu yense kunyumba yake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa