Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 20:11 - Buku Lopatulika

11 Koma Maria analikuima kumanda kunja, alikulira. Ndipo m'mene alikulira anawerama chisuzumirire kumanda;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Koma Maria analikuima kumanda kunja, alikulira. Ndipo m'mene alikulira anawerama chisuzumirire kumanda;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Maria adakhalabe chilili panja pafupi ndi manda, akulira. Akulira choncho, adaŵerama kusuzumira m'mandamo,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 koma Mariya anayima kunja kwa manda akulira. Pamene akulira, anawerama ndi kusuzumira mʼmanda

Onani mutuwo Koperani




Yohane 20:11
2 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene analowa m'manda, anaona mnyamata alikukhala kumbali ya kudzanja lamanja, wovala mwinjiro woyera; ndipo iwo anadabwa.


ndipo m'mene anawerama chosuzumira anaona nsalu zabafuta zitakhala, komatu sanalowemo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa