Yohane 20:6 - Buku Lopatulika6 Pamenepo anadzanso Simoni Petro alikumtsata iye, nalowa m'manda; ndipo anaona nsalu zabafuta zitakhala, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pamenepo anadzanso Simoni Petro alikumtsata iye, nalowa m'manda; ndipo anaona nsalu zabafuta zitakhala, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Simoni Petro atafika akumutsatira, adaloŵa m'mandamo. Adaona nsalu zija zili chikhalire, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Kenaka Simoni Petro, amene anali pambuyo pake, anafika ndi kulowa mʼmanda. Iye anaona nsaluzo zili pamenepo, Onani mutuwo |