Yohane 20:7 - Buku Lopatulika7 ndi mlezo, umene unali pamutu pake, wosakhala pamodzi ndi nsalu zabafuta, koma wopindika padera pamalo pena. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 ndi mlezo, umene unali pamutu pake, wosakhala pamodzi ndi nsalu zabafuta, koma wopindika padera pamalo pena. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 ndiponso kansalu kamene kanali kumutu kwake. Kansaluko sikanali pamodzi ndi nsalu zina zija, koma padera pakokha, kali chipindire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 pamodzinso ndi nsalu imene anakulungira nayo mutu wa Yesu. Nsaluyi inali yopindidwa pa yokha yosiyanitsidwa ndi inayo. Onani mutuwo |