Yohane 20:23 - Buku Lopatulika23 Zochimwa za anthu ali onse muwakhululukira, zikhululukidwa kwa iwo; za iwo amene muzigwiritsa, zagwiritsidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Zochimwa za anthu ali onse muwakhululukira, zikhululukidwa kwa iwo; za iwo amene muzigwiritsa, zagwiritsidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Anthu amene mudzaŵakhululukira machimo ao, adzakhululukidwadi, koma amene simudzaŵakhululukira, sadzakhululukidwa ai.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ngati mukhululukira aliyense machimo ake, iwo akhululukidwa; ngati simuwakhululukira, iwo sanakhululukidwe.” Onani mutuwo |