Yohane 20:24 - Buku Lopatulika24 Koma Tomasi, mmodzi wa khumi ndi awiriwo, wotchedwa Didimo, sanakhale nao pamodzi, pamene Yesu anadza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Koma Tomasi, mmodzi wa khumi ndi awiriwo, wotchedwa Didimo, sanakhala nao pamodzi, pamene Yesu anadza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Mmodzi mwa ophunzira aja khumi ndi aŵiri, Tomasi (wotchedwa Didimo), sanali pamodzi ndi anzake pamene Yesu adaabwera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Koma Tomasi (otchedwa Didimo), mmodzi wa khumi ndi awiriwo, sanali ndi ophunzira pamene Yesu anabwera. Onani mutuwo |