Yohane 2:18 - Buku Lopatulika18 Chifukwa chake Ayuda anayankha nati kwa Iye, Mutionetsera ife chizindikiro chanji, pakuti muchita izi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Chifukwa chake Ayuda anayankha nati kwa Iye, Mutionetsera ife chizindikiro chanji, pakuti muchita izi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Pamenepo akuluakulu a Ayuda adamufunsa kuti, “Kodi mungatiwonetse chizindikiro chotani chakuti muli ndi ulamuliro wochitira zimenezi?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Kenaka Ayuda anamufunsa Yesu kuti, “Kodi mungationetse chizindikiro chodabwitsa chotani chotsimikizira ulamuliro wanu wochitira izi?” Onani mutuwo |