Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 2:17 - Buku Lopatulika

17 Ophunzira ake anakumbukira kuti kunalembedwa, Changu cha pa nyumba yanu chandidya ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ophunzira ake anakumbukira kuti kunalembedwa, Changu cha pa nyumba yanu chandidya ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Ophunzira ake adakumbukira Malembo aja akuti, “Changu chomwe ndimachitira nyumba yanu chidzandiphetsa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Ophunzira ake anakumbukira kuti zinalembedwa kuti, “Kudzipereka kwanga ku nyumba yanu kudzandiphetsa.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 2:17
4 Mawu Ofanana  

Changu changa chinandithera, popeza akundisautsa anaiwala mau anu.


Pakuti changu cha pa nyumba yanu chandidya; ndi zotonza za iwo otonza Inu zandigwera ine.


Ndipo Yesu yemwe ndi ophunzira ake anaitanidwa kuukwatiwo.


Chifukwa chake atauka kwa akufa, ophunzira ake anakumbukira kuti ananena ichi; ndipo anakhulupirira cholemba, ndi mau amene Yesu ananena.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa