Yohane 2:16 - Buku Lopatulika16 nati kwa iwo akugulitsa nkhunda, Chotsani izi muno; musamayesa nyumba ya Atate wanga nyumba ya malonda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 nati kwa iwo akugulitsa nkhunda, Chotsani izi muno; musamayesa nyumba ya Atate wanga nyumba ya malonda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ndipo adalamula ogulitsa nkhunda aja kuti, “Izi zitulutseni muno. Nyumba ya Atate anga musaisandutse nyumba yochitiramo malonda.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Kwa amene amagulitsa nkhunda, Iye anati, “Tulutsani izi muno! Osasandutsa Nyumba ya Atate anga msika!” Onani mutuwo |