Yohane 2:19 - Buku Lopatulika19 Yesu anayankha nati kwa iwo, Pasulani Kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Yesu anayankha nati kwa iwo, Pasulani Kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Yesu adaŵayankha kuti, “Gwetsani nyumba ya Mulungu ino, Ine ndidzaimanganso masiku atatu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Yesu anawayankha kuti, “Gwetsani Nyumba ya Mulunguyi ndipo Ine ndidzayimanganso mʼmasiku atatu.” Onani mutuwo |