Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 19:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo pamene Pilato anamva mau awa, anaopa koposa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo pamene Pilato anamva mau awa, anaopa koposa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Pamene Pilato adamva mau ameneŵa, adachita mantha kwabasi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Pilato atamva zimenezi, anachita mantha kwambiri,

Onani mutuwo Koperani




Yohane 19:8
4 Mawu Ofanana  

Pamenepo Pilato, m'mene adamva mau awa, anatuluka ndi Yesu, nakhala pansi pa mpando woweruzira kumalo dzina lake, Bwalo lamiyala, koma mu Chihebri, Gabata.


Ayuda anamyankha iye, Tili nacho chilamulo ife, ndipo monga mwa chilamulocho ayenera kufa, chifukwa anadziyesera Mwana wa Mulungu.


Ndipo analowanso ku Pretorio, nanena kwa Yesu, Muchoka kuti? Koma Yesu sanamyankhe kanthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa