Yohane 19:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo analowanso ku Pretorio, nanena kwa Yesu, Muchoka kuti? Koma Yesu sanamyankhe kanthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo analowanso ku Pretorio, nanena kwa Yesu, Muchoka kuti? Koma Yesu sanamyankha kanthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsono adaloŵanso m'nyumba ya bwanamkubwa ija nafunsa Yesu kuti, “Kodi iwe, kwanu nkuti?” Koma Yesu sadayankhe kanthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 ndipo anabwereranso mʼnyumba yaufumu. Iye anafunsa Yesu kuti, “Kodi umachokera kuti?” Koma Yesu sanayankhe. Onani mutuwo |