Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 19:22 - Buku Lopatulika

22 Pilato anayankha, Chimene ndalemba, ndalemba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Pilato anayankha, Chimene ndalemba, ndalemba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Koma Pilato adati, “Zimene ndalemba, ndalemba ndatha basi.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Pilato anayankha kuti, “Chimene ine ndalemba, ndalemba.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 19:22
6 Mawu Ofanana  

Mulungu Wamphamvuyonse adzakupatsani inu chifundo pamaso pa munthu uja, kuti akumasulireni inu mbale wanu wina ndi Benjamini. Ndipo ine, ngati ndikhala wopanda ana, ndikhalatu.


Muka, sonkhanitsa Ayuda onse opezeka mu Susa, nimundisalire, osadya osamwa masiku atatu, usiku ndi usana, ine ndemwe ndi anamwali anga tidzasala momwemo, ndipo motero ndidzalowa kwa mfumu, ndiko kosalingana ndi lamulo; ndikaonongeka tsono ndionongeke.


Amene atontholetsa kukuntha kwa nyanja, kukuntha kwa mafunde ake, ndi phokoso la mitundu ya anthu.


Indedi, kuzaza kwake kwa munthu kudzakulemekezani; chotsalira cha kuzazaku mudzachiletsa.


Poikira nyanja malire ake, kuti madzi asapitirire pa lamulo lake; polemba maziko a dziko.


Pa ichi Pilato anafuna kumasula Iye; koma Ayuda anafuula, ndi kunena, Ngati mumasula ameneyo, simuli bwenzi la Kaisara; yense wodziyesera yekha mfumu atsutsana naye Kaisara.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa