Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 19:21 - Buku Lopatulika

21 Pamenepo ansembe aakulu a Ayuda, ananena kwa Pilato, Musalembe, Mfumu ya Ayuda; koma kuti Iyeyu anati, Ndili mfumu ya Ayuda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Pamenepo ansembe aakulu a Ayuda, ananena kwa Pilato, Musalembe, Mfumu ya Ayuda; koma kuti Iyeyu anati, Ndili mfumu ya Ayuda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Akulu a ansembe a Ayuda adauza Pilato kuti, “Musalembe kuti, ‘Mfumu ya Ayuda’ ai, koma kuti, ‘Iyeyu ankati Ndine Mfumu ya Ayuda.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Kenaka mkulu wa ansembe wa Ayuda anakadandaula kwa Pilato nati, “Musalembe kuti ‘Mfumu ya Ayuda,’ koma kuti munthuyu amadzitcha kuti ndi mfumu ya Ayuda.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 19:21
2 Mawu Ofanana  

Koma linali tsiku lokonza Paska; panali monga ora lachisanu ndi chimodzi. Ndipo ananena kwa Ayuda, Taonani, mfumu yanu!


Koma Pilato analemba lembo, naliika pamtanda. Koma panalembedwa, YESU MNAZARAYO, MFUMU YA AYUDA.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa