Yohane 19:18 - Buku Lopatulika18 kumene anampachika Iye; ndipo pamodzi ndi Iye awiri ena, chakuno ndi chauko, koma Yesu pakati. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 kumene anampachika Iye; ndipo pamodzi ndi Iye awiri ena, chakuno ndi chauko, koma Yesu pakati. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Kumeneko adampachika pa mtanda. Adapachikanso anthu ena aŵiri, wina ku dzanja lake lamanja, wina ku dzanja lake lamanzere, Yesu pakati. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Pamenepo iwo anamupachika Iye pamodzi ndi anthu ena awiri, mmodzi mbali ina ndi wina mbali inanso ndipo Yesu pakati. Onani mutuwo |