Yohane 19:19 - Buku Lopatulika19 Koma Pilato analemba lembo, naliika pamtanda. Koma panalembedwa, YESU MNAZARAYO, MFUMU YA AYUDA. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Koma Pilato analemba lembo, naliika pamtanda. Koma panalembedwa, YESU MNAZARAYO, MFUMU YA AYUDA. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Pilato adalemba chidziŵitso nachiika pamtandapo. Adaalembapo kuti, “Yesu wa ku Nazarete, Mfumu ya Ayuda.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Pilato analemba chikwangwani chomwe anachikhoma pa mtandapo. Panalembedwa mawu akuti, yesu wa ku nazareti, mfumu ya ayuda. Onani mutuwo |