Yohane 18:8 - Buku Lopatulika8 Yesu anayankha, Nati, Ndine; chifukwa chake ngati mufuna Ine, lekani awa amuke; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Yesu anayankha, Nati, Ndine; chifukwa chake ngati mufuna Ine, lekani awa amuke; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Yesu adati, “Ndakuuzani kuti ndine, ndilipo. Tsono ngati mukufuna Ine, aŵa alekeni apite.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Yesu anayankha kuti, “Ine ndakuwuzani kuti Ndine. Ngati inu mukufuna Ine, asiyeni anthu awa apite.” Onani mutuwo |