Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 18:7 - Buku Lopatulika

7 Pamenepo anawafunsanso, Mufuna yani? Koma iwo anati, Yesu Mnazarayo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Pamenepo anawafunsanso, Mufuna yani? Koma iwo anati, Yesu Mnazarayo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Yesu adaŵafunsanso kuti, “Mukufuna yani kodi?” Iwo aja adati “Tikufuna Yesu wa ku Nazarete.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Iye anawafunsanso kuti, “Kodi mukumufuna ndani?” Ndipo iwo anati, “Yesu wa ku Nazareti.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 18:7
4 Mawu Ofanana  

nadza nakhazikika m'mzinda dzina lake Nazarete kuti chikachitidwe chonenedwa ndi aneneri kuti, Adzatchedwa Mnazarayo.


Pamenepo Yesu, podziwa zonse zilinkudza pa Iye, anatuluka, nati kwa iwo, Mufuna yani?


Ndipo m'mene anati kwa iwo, Ndine, anabwerera m'mbuyo, nagwa pansi.


Yesu anayankha, Nati, Ndine; chifukwa chake ngati mufuna Ine, lekani awa amuke;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa