Yohane 18:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo m'mene anati kwa iwo, Ndine, anabwerera m'mbuyo, nagwa pansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo m'mene anati kwa iwo, Ndine, anabwerera m'mbuyo, nagwa pansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pamene Yesu adaŵayankha kuti, “Ndine, ndilipo,” iwo adabwerera m'mbuyo nagwa pansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pamene Yesu anati, “Ndine,” iwo anabwerera mʼmbuyo ndi kugwa pansi. Onani mutuwo |