Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 18:9 - Buku Lopatulika

9 kuti akwaniridwe mau amene ati, Mwa iwo amene mwandipatsa Ine, sindinataye mmodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 kuti akwaniridwe mau amene ati, Mwa iwo amene mwandipatsa Ine, sindinataya mmodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 (Adaatero kuti zipherezere zimene Iye adaanena kale kuti, “Sindidatayepo ndi mmodzi yemwe mwa amene mudandipatsa.”)

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Izi zinachitika kuti mawu amene Iye anayankhula akwaniritsidwe: “Ine sindinataye ndi mmodzi yemwe mwa iwo amene mwandipatsa.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 18:9
3 Mawu Ofanana  

Pamene ndinakhala nao, Ine ndinalikuwasunga iwo m'dzina lanu amene mwandipatsa Ine; ndipo ndinawasunga, ndipo sanatayike mmodzi yense wa iwo, koma mwana wa chitayiko, kuti lembo likwaniridwe.


Yesu anayankha, Nati, Ndine; chifukwa chake ngati mufuna Ine, lekani awa amuke;


Koma chifuniro cha Iye amene anandituma Ine ndi ichi, kuti za ichi chonse Iye anandipatsa Ine ndisatayeko kanthu, koma ndichiukitse tsiku lomaliza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa