Yohane 18:30 - Buku Lopatulika30 Anayankha nati kwa iye, Akadakhala wosachita zoipa uyu sitikadampereka Iye kwa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Anayankha nati kwa iye, Akadakhala wosachita zoipa uyu sitikadampereka Iye kwa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Iwo adati, “Akadapanda kuchita choipa ameneyu, sibwenzi titadzampereka kwa inu ai.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Iwo anayankha kuti, “Ngati Iye akanakhala kuti si wolakwa, ife sitikanamupereka kwa inu.” Onani mutuwo |