Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 18:29 - Buku Lopatulika

29 Chifukwa chake Pilato anatulukira kunja kwa iwo, nati, Chifukwa chanji mwadza nacho cha munthu uyu?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Chifukwa chake Pilato anatulukira kunja kwa iwo, nati, Chifukwa chanji mwadza nacho cha munthu uyu?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Motero Pilato adatulukira kwa iwo naŵafunsa kuti, “Mwampeza cholakwa chanji munthuyu?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Choncho Pilato anatuluka napita kwa iwo ndipo anati, “Kodi ndi milandu yanji imene mukumuzenga munthu uyu?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 18:29
9 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anati, Chifukwa ninji? Anachita choipa chotani? Koma iwo anafuulitsa kopambana, Apachikidwe pamtanda.


Anayankha nati kwa iye, Akadakhala wosachita zoipa uyu sitikadampereka Iye kwa inu.


Chifukwa chake Pilato analowanso mu Pretorio, naitana Yesu, nati kwa Iye, Iwe ndiwe mfumu ya Ayuda kodi?


Koma ndinawayankha, kuti machitidwe a Aroma satero, kupereka munthu asanayambe woneneredwayo kupenyana nao omnenera ndi kukhala napo podzikanira pa chomneneracho.


Pakuti zoonadi anasonkhanidwa m'mzinda muno Herode, ndi Pontio Pilato yemwe pamodzi ndi amitundu ndi anthu a Israele kumchitira choipa Mwana wanu wopatulika Yesu amene munamdzoza;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa