Yohane 18:14 - Buku Lopatulika14 Koma Kayafa anali uja wakulangiza Ayuda, kuti kuyenera munthu mmodzi afere anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma Kayafa anali uja wakulangiza Ayuda, kuti kuyenera munthu mmodzi afere anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Kayafayo ndi yemwe uja amene adaalangiza anzake kuti nkwabwino koposa kuti munthu mmodzi afe m'malo mwa anthu onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Kayafa anali amene analangiza Ayuda kuti kukanakhala kwabwino ngati munthu mmodzi akanafera anthu. Onani mutuwo |