Yohane 18:13 - Buku Lopatulika13 nayamba kupita naye kwa Anasi; pakuti anali mpongozi wa Kayafa, amene anali mkulu wa ansembe chaka chomwecho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 nayamba kupita naye kwa Anasi; pakuti anali mpongozi wa Kayafa, amene anali mkulu wa ansembe chaka chomwecho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Poyamba adapita naye kwa Anasi, chifukwa anali mpongozi wa Kayafa, amene anali mkulu wa ansembe onse chaka chimenecho. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Poyamba anapita naye kwa Anasi amene anali mkamwini wa Kayafa, mkulu wa ansembe chaka chimenecho. Onani mutuwo |