Yohane 17:8 - Buku Lopatulika8 chifukwa mau amene munandipatsa Ine ndinapatsa iwo; ndipo analandira, nazindikira koona kuti ndinatuluka kwa Inu, ndipo anakhulupirira kuti Inu munandituma Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 chifukwa mau amene munandipatsa Ine ndinapatsa iwo; ndipo analandira, nazindikira koona kuti ndinatuluka kwa Inu, ndipo anakhulupirira kuti Inu munandituma Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Pakuti ndaŵapatsa mau amene mudandiwuza Ine, ndipo aŵalandira. Akudziŵadi kuti ndidachokera kwa Inu, ndipo sakayika kuti ndinu mudandituma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Pakuti Ine ndiwapatsa mawu amene Inu munandipatsa ndipo awalandira. Iwo akudziwa ndithu kuti Ine ndinachokera kwa Inu, ndipo akukhulupirira kuti Inu ndiye amene munandituma Ine. Onani mutuwo |