Yohane 17:7 - Buku Lopatulika7 Azindikira tsopano kuti zinthu zilizonse zimene mwandipatsa Ine zichokera kwa Inu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Azindikira tsopano kuti zinthu zilizonse zimene mwandipatsa Ine zichokera kwa Inu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsopano akudziŵa kuti zonse zimene mudandipatsa nzochokera kwa Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Tsopano akudziwa kuti zonse zimene munandipatsa nʼzochokera kwa Inu. Onani mutuwo |