Yohane 17:6 - Buku Lopatulika6 Ndalionetsera dzina lanu kwa anthu amene mwandipatsa Ine m'dziko lapansi; anali anu, ndipo mwandipatsa Ine iwo; ndipo adasunga mau anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndalionetsera dzina lanu kwa anthu amene mwandipatsa Ine m'dziko lapansi; anali anu, ndipo mwandipatsa Ine iwo; ndipo adasunga mau anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Amene mudaŵapatula mwa anthu onse ndi kundipatsa Ine, ndaŵadziŵitsa dzina lanu. Anali anu, Inu mudaŵapereka kwa Ine, ndipo adasunga mau anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “Ine ndawadziwitsa za Inu anthu amene munandipatsa mʼdziko lapansi. Iwo anali anu. Inu munawapereka kwa Ine ndipo amvera mawu anu. Onani mutuwo |