Yohane 17:3 - Buku Lopatulika3 Koma moyo wosatha ndi uwu, kuti akadziwe Inu Mulungu woona yekha, ndi Yesu Khristu amene munamtuma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma moyo wosatha ndi uwu, kuti akadziwe Inu Mulungu woona yekha, ndi Yesu Khristu amene munamtuma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Moyo wosathawo ndi wakuti akudziŵeni Inu, amene nokhanu ndinu Mulungu weniweni, ndipo adziŵenso Yesu Khristu amene mudamtuma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tsono moyo wosathawo ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma. Onani mutuwo |