Yohane 17:2 - Buku Lopatulika2 monga mwampatsa Iye ulamuliro pa thupi lililonse, kuti onse amene mwampatsa Iye, awapatse iwo moyo wosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 monga mwampatsa Iye ulamuliro pa thupi lililonse, kuti onse amene mwampatsa Iye, awapatse iwo moyo wosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pajatu mudampatsa mphamvu zolamulira anthu onse, kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mudampatsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Pakuti Inu munamupatsa Iye ulamuliro pa anthu onse kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mwamupatsa. Onani mutuwo |