Yohane 17:1 - Buku Lopatulika1 Zinthu izi analankhula Yesu; ndipo m'mene anakweza maso ake Kumwamba, anati, Atate, yafika nthawi; lemekezani Mwana wanu, kuti Mwana wanu akulemekezeni Inu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Zinthu izi analankhula Yesu; ndipo m'mene anakweza maso ake Kumwamba, anati, Atate, yafika nthawi; lemekezani Mwana wanu, kuti Mwana wanu akulemekezeni Inu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Yesu atanena zimenezi, adayang'ana kumwamba nati, “Atate, yafika nthaŵi. Lemekezani Mwana wanu, kuti Mwanayo akulemekezeni Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yesu atatha kunena izi, anayangʼana kumwamba ndipo anapemphera: “Atate, nthawi yafika. Lemekezani Mwana wanu, kuti Mwana wanuyo akulemekezeni Inu. Onani mutuwo |