Yohane 17:4 - Buku Lopatulika4 Ine ndalemekeza Inu padziko lapansi, m'mene ndinatsiriza ntchito imene munandipatsa ndichite. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ine ndalemekeza Inu pa dziko lapansi, m'mene ndinatsiriza ntchito imene munandipatsa ndichite. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndakulemekezani pansi pano pakutsiriza ntchito imene mudandipatsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ine ndabweretsa ulemerero wanu pa dziko pamene ndamaliza ntchito imene munandipatsa kuti ndi igwire. Onani mutuwo |