Yohane 17:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo chifukwa cha iwo Ine ndidzipatula ndekha kuti iwonso akhale opatulidwa m'choonadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo chifukwa cha iwo Ine ndidzipatula ndekha kuti iwonso akhale opatulidwa m'choonadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ndipo chifukwa cha iwoŵa ndikudzipereka kwa Inu, kuti iwonso akhale odzipereka moonadi kwa Inu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Chifukwa cha iwowa Ine ndikudziyeretsa, kuti iwo ayeretsedwenso kwenikweni. Onani mutuwo |