Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 17:20 - Buku Lopatulika

20 Koma sindipempherera iwo okha, komanso iwo akukhulupirira Ine chifukwa cha mau ao;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Koma sindipempherera iwo okha, komanso iwo akukhulupirira Ine chifukwa cha mau ao;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 “Sindikupempherera iwo okhaŵa ai, komanso amene adzandikhulupirira chifukwa cha mau ao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 “Ine sindikupempherera iwo okhawa, komanso amene adzandikhulupirira chifukwa cha uthenga wawo.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 17:20
10 Mawu Ofanana  

Ndipo nkhosa zina ndili nazo, zimene sizili za khola ili; izinso ndiyenera kuzitenga, ndipo zidzamva mau anga; ndipo zidzakhala gulu limodzi, mbusa mmodzi.


Ndipo chifukwa cha iwo Ine ndidzipatula ndekha kuti iwonso akhale opatulidwa m'choonadi.


kuti onse akakhale amodzi, monga Inu Atate mwa Ine, ndi Ine mwa Inu, kuti iwonso akakhale mwa Ife: kuti dziko lapansi likakhulupirire kuti Inu munandituma Ine.


Pamenepo iwo amene analandira mau ake anabatizidwa; ndipo anaonjezedwa tsiku lomwelo anthu ngati zikwi zitatu.


Koma ambiri a iwo amene adamva mau anakhulupirira; ndipo chiwerengero cha amuna chinali ngati zikwi zisanu.


koma chaonetsedwa tsopano, ndi kudziwidwa kwa anthu a mitundu yonse mwa malembo a aneneriwo, monga mwa lamulo la Mulungu wosatha, kuti amvere chikhulupiriro;


Ndipo Iye anapatsa ena akhale atumwi; ndi ena aneneri; ndi ena alaliki; ndi ena abusa, ndi ena aphunzitsi;


kwa Timoteo, mwana wanga wokondedwa: Chisomo, chifundo, mtendere za kwa Mulungu Atate ndi Khristu Yesu Ambuye wathu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa