Yohane 17:20 - Buku Lopatulika20 Koma sindipempherera iwo okha, komanso iwo akukhulupirira Ine chifukwa cha mau ao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Koma sindipempherera iwo okha, komanso iwo akukhulupirira Ine chifukwa cha mau ao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 “Sindikupempherera iwo okhaŵa ai, komanso amene adzandikhulupirira chifukwa cha mau ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 “Ine sindikupempherera iwo okhawa, komanso amene adzandikhulupirira chifukwa cha uthenga wawo. Onani mutuwo |