Yohane 17:18 - Buku Lopatulika18 Monga momwe munandituma Ine kudziko lapansi, Inenso ndinatuma iwo kudziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Monga momwe munandituma Ine kudziko lapansi, Inenso ndinatuma iwo kudziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Monga mudandituma Ine pansi pano, Inenso ndaŵatuma pansi pano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Monga Inu munandituma Ine mʼdziko lapansi, Inenso ndikuwatuma mʼdziko lapansi. Onani mutuwo |