Yohane 17:17 - Buku Lopatulika17 Patulani iwo m'choonadi; mau anu ndi choonadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Patulani iwo m'choonadi; mau anu ndi choonadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Muziŵapatula ndi mau anu kuti akhale anthu anu. Mau anuwo ngoona zedi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ayeretseni ndi choonadi chanu. Mawu anu ndiye choonadi. Onani mutuwo |