Yohane 16:26 - Buku Lopatulika26 Tsiku limenelo mudzapempha m'dzina langa; ndipo sindinena kwa inu kuti Ine ndidzafunsira inu kwa Atate; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Tsiku limenelo mudzapempha m'dzina langa; ndipo sindinena kwa inu kuti Ine ndidzafunsira inu kwa Atate; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Tsiku limenelo mudzapempha potchula dzina langa, ndipo sindikuti Ine ndidzakupempherani kwa Atate ai, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Tsiku limenelo inu mudzapempha mʼdzina langa. Ine sindikunena kuti ndidzapempha Atate mʼmalo mwanu ayi. Onani mutuwo |