Yohane 16:16 - Buku Lopatulika16 Katsala kanthawi, ndipo simundionanso Ine, ndipo kanthawinso, ndipo mudzandiona Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Katsala kanthawi, ndipo simundionanso Ine, ndipo kanthawinso, ndipo mudzandiona Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 “Kanthaŵi pang'ono ndipo simudzandiwonanso, koma patapitanso kanthaŵi pang'ono, mudzandiwona.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Yesu anapitiriza kuyankhula kuti, “Mwa kanthawi kochepa, simudzandionanso, ndipo patatha nthawi pangʼono mudzandionanso.” Onani mutuwo |