Yohane 16:14 - Buku Lopatulika14 Iyeyo adzalemekeza Ine; chifukwa adzatenga za mwa Ine, nadzalalikira kwa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Iyeyo adzalemekeza Ine; chifukwa adzatenga za mwa Ine, nadzalalikira kwa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Adzandilemekeza, pakuti adzatenga zochokera kwa Ine nadzakudziŵitsani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Iye adzalemekeza Ine chifukwa adzatenga za Ine nadzakudziwitsani. Onani mutuwo |