Yohane 16:12 - Buku Lopatulika12 Ndili nazo zambirinso zakunena kwa inu, koma simungathe kuzisenza tsopano lino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndili nazo zambirinso zakunena kwa inu, koma simungathe kuzisenza tsopano lino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 “Ndili nawo mau ena ambiri oti ndikuuzeni, koma simungathe kuŵamvetsa tsopano ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “Ine ndili ndi zambiri zoti ndiyankhule nanu, koma simungathe kuzilandira tsopano. Onani mutuwo |