Yohane 16:11 - Buku Lopatulika11 za chiweruzo, chifukwa mkulu wa dziko ili lapansi waweruzidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 za chiweruzo, chifukwa mkulu wa dziko ili lapansi waweruzidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ngolakwa pa za kuweruza, chifukwa Satana, mfumu ya anthu oipa a dziko lino lapansi, waweruzidwa kale. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Za chiweruzo, chifukwa wolamulira dziko lino lapansi waweruzidwa tsopano. Onani mutuwo |