Yohane 16:10 - Buku Lopatulika10 za chilungamo, chifukwa ndinka kwa Atate, ndipo simundionanso; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 za chilungamo, chifukwa ndinka kwa Atate, ndipo simundionanso; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ngolakwa pa za kulungama, chifukwa ndikupita kwa Atate ndipo simudzandiwonanso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Za chilungamo, chifukwa Ine ndi kupita kwa Atate, kumene simudzandionanso. Onani mutuwo |