Yohane 15:9 - Buku Lopatulika9 Monga momwe Atate wandikonda Ine, Inenso ndakonda inu; khalani m'chikondi changa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Monga momwe Atate wandikonda Ine, Inenso ndakonda inu; khalani m'chikondi changa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Monga momwe Atate andikondera, Inenso ndakukondani. Muzikhala m'chikondi changachi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Monga momwe Atate amandikondera Ine, Inenso ndakukondani. Tsopano khalani mʼchikondi changa. Onani mutuwo |