Yohane 15:8 - Buku Lopatulika8 Mwa ichi alemekezedwa Atate wanga, kuti mubale chipatso chambiri; ndipo mudzakhala ophunzira anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Mwa ichi alemekezedwa Atate wanga, kuti mubale chipatso chambiri; ndipo mudzakhala ophunzira anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Atate anga amalemekezedwa pamene mubereka zipatso zambiri, ndipo pakutero mumaonetsa kuti ndinu ophunzira anga enieni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Atate anga amalemekezedwa mukamabereka zipatso zochuluka, ndipo potero mudzionetsa kuti ndinu ophunzira anga. Onani mutuwo |