Yohane 15:7 - Buku Lopatulika7 Ngati mukhala mwa Ine, ndi mau anga akhala mwa inu, pemphani chilichonse chimene muchifuna ndipo chidzachitika kwa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ngati mukhala mwa Ine, ndi mau anga akhala mwa inu, pemphani chilichonse chimene muchifuna ndipo chidzachitika kwa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ngati mukhala mwa Ine, ndipo mau anga akhala mwa inu, mupemphe chilichonse chimene mungachifune, ndipo mudzachilandiradi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ngati inu mukhala mwa Ine ndipo mawu anga akhala mwa inu, pemphani chilichonse chimene mukufuna ndipo mudzapatsidwa. Onani mutuwo |