Yohane 15:22 - Buku Lopatulika22 Sindikadadza ndi kulankhula nao sakadakhala nalo tchimo; koma tsopano alibe chowiringula pa machimo ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Sindikadadza ndi kulankhula nao sakadakhala nalo tchimo; koma tsopano alibe chowiringula pa machimo ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ndikadapanda kubwera ndi kulankhula nawo, sakadakhala ndi mlandu. Koma tsopano alibe choti nkukanira mlandu wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ine ndikanapanda kubwera ndi kuyankhula nawo, sakanakhala ndi mlandu. Koma tsopano alibe choti nʼkukanira mlandu wawo. Onani mutuwo |