Yohane 15:21 - Buku Lopatulika21 Koma izi zonse adzakuchitirani chifukwa cha dzina langa, chifukwa sadziwa wondituma Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Koma izi zonse adzakuchitirani chifukwa cha dzina langa, chifukwa sadziwa wondituma Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Koma adzakuchitirani zonsezi chifukwa cha Ine, popeza kuti samdziŵa amene adandituma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Iwo adzakuchitani zimenezi chifukwa cha dzina langa, popeza sakudziwa amene anandituma Ine. Onani mutuwo |