Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 15:23 - Buku Lopatulika

23 Iye wondida Ine, adanso Atate wanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Iye wondida Ine, adanso Atate wanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Munthu wodana ndi Ine, amadana ndi Atate anganso.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Iye amene amadana ndi Ine amadananso Atate anga.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 15:23
5 Mawu Ofanana  

Sindikadadza ndi kulankhula nao sakadakhala nalo tchimo; koma tsopano alibe chowiringula pa machimo ao.


Sindikadachita mwa iwo ntchito zosachita wina, sakadakhala nalo tchimo; koma tsopano anaona, nada Ine ndi Atate wanganso.


Yense wakukana Mwana, alibe Atate; wovomereza Mwana ali ndi Atatenso.


Yense wakupitirira, wosakhala m'chiphunzitso cha Khristu, alibe Mulungu; iye wakukhala m'chiphunzitso, iyeyo ali nao Atate ndi Mwana.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa