Yohane 14:7 - Buku Lopatulika7 Mukadazindikira Ine mukadadziwa Atate wanganso; kuyambira tsopano mumzindikira Iye, ndipo mwamuona Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Mukadazindikira Ine mukadadziwa Atate wanganso; kuyambira tsopano mumzindikira Iye, ndipo mwamuona Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Mukadandidziŵa Ine, Atate anganso mukadaŵadziŵa. Kuyambira tsopano mukuŵadziŵa ndipo mwaŵaona.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Mukanandidziwadi Ine, mukanadziwanso Atate anga. Kuyambira tsopano, mukuwadziwa ndipo mwawaona.” Onani mutuwo |